John 19:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma pamene adafika pa Yesu, poona kuti wafa kale, sadathyole miyendo yake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
koma pofika kwa Yesu, m'mene anamuona Iye, kuti wafa kale, sanathyola miyendo yake;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma atafika pa Yesu ndi kupeza kuti anali atamwalira kale, iwo sanathyole miyendo yake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
koma pofika kwa Yesu, m'mene anamuona iye, kuti wafa kale, sanatyola miyendo yace;