John 2:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Yesu ankanena za thupi lake mophiphiritsa, pamene adaatchula Nyumba ya Mulungu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Iye analikunena za Kachisi wa thupi lake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Nyumba ya Mulungu imene amanena linali thupi lake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma iye analikunena za kacisi wathupi lace.