John 2:24 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Yesu sadaikepo chikhulupiriro pa iwowo, popeza kuti Iye ankaŵadziŵa anthu onse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Yesu sanakhulupirire iwo kuti akhale nao, chifukwa Iye anadziwa anthu onse,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Yesu sanawakhulupirire iwo, pakuti amadziwa anthu onse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Yesu sanakhulupirira iwo kuti akhale nao, cifukwa iye anadziwa anthu onse,