John 20:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tomasi adati, “Ambuye anga! Mulungu wanga!”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tomasi anayankha nati kwa Iye, Ambuye wanga, ndi Mulungu wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tomasi anati kwa Iye, “Ambuye wanga ndi Mulungu wanga!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tomasi anayankha nati kwa iye, Ambuye wanga, ndi Mulungu wanga.