John 20:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo Petro ndi wophunzira wina uja adatuluka napita ku manda.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anatuluka tsono Petro ndi wophunzira winayo, nalinkupita kumanda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho Petro ndi wophunzira winayo ananyamuka kupita ku manda.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anaturuka tsono Petro ndi wophunzira winayo, nalinkupita kumanda.