John 20:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mpaka nthaŵi imeneyo iwo aja anali asanamvetse Malembo akuti Yesu adzayenera kuuka kwa akufa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti kufikira pomwepo sanadziwa lembo lakuti ayenera Iye kuuka kwa akufa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
(Iwo sanazindikire kuchokera mʼmalemba kuti Yesu anayanera kuuka kuchokera kwa akufa).
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti kufikira pomwepo sanadziwa lembo lakuti ayenera iye kuuka kwa akufa.