John 21:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adaŵauza kuti, “Bwera nazoni nsomba zina zimene mwapha.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesu ananena nao, Tenganiko nsomba zimene mwazigwira tsopano.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anawawuza kuti, “Tabweretsa nsomba zina mwagwirazo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesu ananena nao, Tenganiko nsomba zimene mwazigwira tsopano,