John 21:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Aka nkachitatu kuti Yesu aonekere ophunzira ake Iye atauka kwa akufa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Imeneyo ndi nthawi yachitatu yakudzionetsera Yesu kwa ophunzira ake, m'mene atauka kwa akufa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Aka kanali tsopano kachitatu Yesu akuonekera kwa ophunzira ake Iye ataukitsidwa kwa akufa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Imeneyo ndi nthawi yacitatu yakudzionetsera Yesu kwa akuphunzira ace, m'mene atauka kwa akufa.