John 21:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
(Yesu adanena zimenezi pofuna kuŵadziŵitsa za m'mene Petro adzafere ndi kulemekeza Mulungu.) Atatero, adauza Petro kuti, “Unditsate.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ichi ananena ndi kuzindikiritsa imfa imene adzalemekeza nayo Mulungu. Ndipo m'mene ananena ichi, anati kwa iye, Nditsate Ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu ananena izi kumuzindikiritsa mtundu wa imfa imene Petro adzalemekezera nayo Mulungu. Kenaka Iye anati kwa Petro, “Nditsate Ine!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ici ananena ndi kuzindikiritsa imfa imene adzalemekeza nayo Mulungu. Ndipo m'mene ananena ici, anati kwa iye, nditsate Ine,