John 21:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Iye adaŵafunsa kuti, “Kodi anzathu, mwaphako kanthu ngati?” Iwo adati, “Ai ndithu, tabwera chabe.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesu ananena nao, Ananu, muli nako kanthu kakudya kodi? Anamyankha Iye, Iai.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anawafunsa iwo kuti, “Anzanga, kodi muli nsomba?” Iwo anayankha kuti, “Ayi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesu ananena nao, Ananu, muli nako kanthu kakudya kodi? Anamyankha iye, lai.