John 3:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adati, “Kodi iwe sindiwe mphunzitsi wodziŵika pakati pa Aisraele, nanga sukumvetsa bwanji zimenezi?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesu anayankha nati kwa iye, Kodi uli mphunzitsi wa Israele, ndipo sudziwa izi?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anati, “Iwe mphunzitsi wa Israeli, kodi sukuzindikira zimenezi?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesu anayankha nati kwa iye, Kodi uli mphunzitsi wa Israyeli, ndipo sudziwa izi?