John 3:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yohane nayenso ankabatiza ku Ainoni pafupi ndi Salimu, chifukwa kumeneko kunali madzi ambiri. Anthu ankafikako, iye nkumaŵabatiza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yohane analinkubatiza m'Ainoni pafupi pa Salimu, chifukwa panali madzi ambiri pamenepo; ndipo analinkufikako anthu, nalinkubatizidwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Yohane amabatizanso ku Ainoni kufupi ndi Salimu, chifukwa kumeneko kunali madzi ambiri ndipo anthu amabwererabwererabe kudzabatizidwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yohane analinkubatiza m'Ainoni pafupi pa Salemu, cifukwa panali madzi ambiri pamenepo; ndipo analinkufikako anthu, nalinkubatizidwa.