John 3:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Usadabwe m'mene ndakuuza kuti muyenera kubadwanso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Usadabwe chifukwa ndinati kwa iwe, Uyenera kubadwa mwatsopano.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwe usadabwe chifukwa ndakuwuza kuti, ‘Uyenera kubadwanso.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Usadabwe cifukwa ndinati kwa iwe, Uyenera kubadwa mwatsopano.