John 4:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Afarisi adamva kuti Yesu akukopa ndi kubatiza ophunzira ambiri koposa Yohane.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake pamene Ambuye anadziwa kuti Afarisi adamva kuti Yesu anayesa anthu ophunzira, nawabatiza koposa Yohane
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu atazindikira kuti Afarisi amva zoti Iye ankapeza ndi kubatiza ophunzira ambiri kupambana Yohane,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace pamene Ambuye anadziwa kuti Afarisi adamva kuti Yesu anayesa anthu ophunzira, nawabatiza koposa Yohane