John 4:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adati, “Pitani mukaitane amuna anu, nkukabweranso kuno.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesu ananena kwa iye, Muka, kamuitane mwamuna wako, nudze kuno.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anamuwuza kuti, “Pita kayitane mwamuna wako ndipo ubwere naye.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesu ananena kwa iye, Muka, kamuitane mwamuna wako, nudze kuno.