John 4:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene Yesu adadziŵa kuti Afarisi azimva zimenezi, adachokako ku Yudeya napitanso ku Galileya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
anachokera ku Yudeya, namukanso ku Galileya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye anachoka ku Yudeya ndi kubwereranso ku Galileya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
anacokera ku Yudeya, namukanso ku Galileya.