John 4:44 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwiniwakeyo anali atanena kuti, “Mneneri, anthu akwao samchitira ulemu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Yesu mwini anachita umboni kuti, Mneneri alibe ulemu m'dziko la kwao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
(Tsopano Yesu mwini ananena kale kuti mneneri salandira ulemu mʼdziko lake).
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Yesu mwini anacita umboni kuti, Mneneri alibe ulemu m'dziko la kwao.