John 5:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musadabwe nazo zimenezi, pakuti ikudza nthaŵi pamene anthu onse amene ali m'manda adzamva mau ake nadzatuluka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Musazizwe ndi ichi, kuti ikudza nthawi, imene onse ali m'manda adzamva mau ake,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Musadabwe ndi zimenezi. Pakuti nthawi ikubwera pamene onse amene ali mʼmanda adzamva mawu ake
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Musazizwe ndi ici, kuti ikudza nthawi, imene onse ali m'manda adzamva mau ace,