John 5:34 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sikuti Ine ndikudalira umboni wa munthu, koma ndikunena izi kuti inu mupulumuke.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Ine sindilandira umboni kwa munthu: koma ndinena izi, kuti inu mukapulumutsidwe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sikuti Ine ndikudalira umboni wa munthu; koma ndikunena zimenezi kuti mupulumutsidwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Ine sindilandira umboni kwa munthu: koma ndinena izi, kuti inu mukapulumutsidwe.