John 5:38 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mau ao sakhala mwa inu, chifukwa simumkhulupirira amene Atatewo adamtuma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mulibe mau ake okhala mwa inu; chifukwa kuti amene Iyeyu anatuma, inu simumkhulupirira ameneyo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kapena mawu ake kukhala mwa inu, pakuti simukhulupirira Iye amene anamutuma.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mulibe mau ace okhala mwa inu; cifukwa kuti amene Iyeyu anatuma, inu simumkhulupirira ameneyo.