John 5:47 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma ngati simukhulupirira zimene iyeyo adalemba, nanga mungakhulupirire bwanji mau anga?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma ngati simukhulupirira malembo a iyeyu, mudzakhulupirira bwanji mau anga?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati simukhulupirira zimene iye analemba, mudzakhulupirira bwanji zimene Ine ndikunena?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma ngati simukhulupirira malembo a iyeyu, mudzakhulupirira bwanji mau anga?