John 6:68 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Simoni Petro adati “Ambuye, nanga tingapitenso kwa yani? Muli nawo ndinu mau opatsa moyo wosatha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Simoni Petro anamyankha Iye, Ambuye, tidzamuka kwa yani? Inu muli nao mau a moyo wosatha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Simoni Petro anamuyankha Iye kuti, “Ambuye, ife tidzapita kwa yani? Inu muli ndi mawu amoyo wosatha.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Simoni Petro anamyankha iye, Ambuye, tidzamuka kwa yani? Inu muli nao mau a moyo wosatha.