John 7:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesu adati, “Ndinangochita ntchito yozizwitsa imodzi yokha, nonsenu nkumadabwa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yesu anayankha nati kwa iwo, Ndinachita ntchito imodzi, ndipo muzizwa monse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anawawuza kuti, “Ine ndinachita chodabwitsa chimodzi ndipo inu mwadabwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yesu anayankha nati kwa iwo, Ndinacita nchito imodzi, ndipo muzizwa monse,