John 7:33 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Apo Yesu adati, “Ndili nanube kanthaŵi pang'ono ndisanapite kwa Atate amene adandituma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo Yesu anati, Katsala kanthawi ndili ndi inu, ndipo ndimuka kwa Iye wondituma Ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yesu anati, “Ine ndili ndi inu kwa kanthawi kochepa chabe, ndipo kenaka ndizipita kwa Iye amene anandituma Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo Yesu anati, Katsala kanthawi ndiri ndi inu, ndipo ndimuka kwa iye wondituma Ine.