John 8:36 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono ngati Mwana akumasulani, mudzakhaladi mfulu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake ngati Mwana adzakuyesani inu aufulu, mudzakhala mfulu ndithu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Nʼchifukwa chake ngati Mwana adzakumasulani, mudzakhala mfulu ndithu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace ngati Mwana adzakuyesani inu aufulu, mudzakhala mfulu ndithu.