John 8:51 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndithu ndikunenetsa kuti munthu akamvera mau anga, sadzafa konse.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Munthu akasunga mau anga, sadzaona imfa nthawi yonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Indetu, indetu, ndinena ndi inu, 9 Munthu akasunga mau anga, sadzaona imfa nthawi yonse.