John 9:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthuwo adamufunsa kuti, “Iyeyo ali kuti?” Munthu uja adati, “Kaya, sindikudziŵa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anamufunsa iye kuti, “Ali kuti munthu ameneyu?” Iye anati, “Ine sindikudziwa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anati kwa iye, Ali kuti Iyeyo? Anena, Sindidziwa ine.