John 9:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono munthu uja kale sankapenyayu adapita naye kwa Afarisi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Anapita naye amene anali wosaona kale kwa Afarisi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo anabwera naye munthu amene poyamba anali wosaona kwa Afarisi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Anapita naye amene anali wosaona kale kwa Afarisi.