Jonah 2:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamene ndidati, ‘Mwanditaya kutali ndi Inu. Kodi ndidzaiyang'ananso bwanji Nyumba yanu yoyera?’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndinati, Ndatayika ndichoke pamaso panu; koma ndidzapenyanso Kachisi wanu wopatulika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinati, ‘Ine ndachotsedwa pamaso panu; komabe ndidzayangʼananso ku Nyumba yanu yopatulika.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndinati, Ndatayika ndicoke pamaso panu; Koma ndidzapenyanso Kacisi wanu wopatulika.