Jonah 2:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Poona kuti ine nkufatu kuno, ndidakumbukira Inu Chauta, pemphero langa lidakufikani m'Nyumba yanu yoyera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pokomoka moyo wanga m'kati mwanga ndinakumbukira Yehova; ndi pemphero langa linafikira Inu m'Kachisi wanu wopatulika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Pamene moyo wanga umachoka mwa ine, ine ndinakumbukira Inu Yehova, ndipo pemphero langa linafika kwa inu, ku Nyumba yanu yopatulika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pokomoka moyo wanga m'kati mwanga ndinakumbukila Yehova; Ndi pemphero langa linafikira Inu m'Kacisi wanu wopatulika.