Jonah 3:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adalankhula ndi Yona kachiŵiri, namuuza kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona nthawi yachiwiri, ndi kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Yehova anayankhula ndi Yona kachiwiri kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo mau a Yehova anadza kwa Yona nthawi yaciwiri, ndi kuti,