Jonah 3:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Nyamuka, pita ku Ninive, mzinda waukulu uja, ukaulalikire uthenga umene ndikukuuza.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nyamuka, pita ku Ninive mudzi waukulu uja, nuulalikire uthenga umene ndikuuza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Nyamuka, pita ku mzinda waukulu wa Ninive ndipo ukalalikire uthenga umene ndikupatsa.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nyamuka, pita ku Nineve mudzi waukuru uja, nuulalikire uthenga umene ndikuuza.