Jonah 4:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chifukwa cha zimenezi Yona adakhumudwa kwambiri, nakwiya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma sikudakomera Yona konse, ndipo anapsa mtima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Yona anakhumudwa kwambiri ndipo anakwiya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma sikudakomera Yona konse, ndipo anapsa mtima.