Joshua 1:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo Yoswa adalamula atsogoleri a Aisraele naŵauza kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo Yoswa analamulira akapitao a anthu, ndi kuti,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Yoswa analamula atsogoleri a Aisraeli nawawuza kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo Yoswa analamulira akapitao a anthu, ndi kuti,