Joshua 1:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Aliyense wokangana ndi inu kapena wosamvera malamulo anu, adzaphedwa. Inu mukhale amphamvu, ndipo mulimbe mtima kwambiri.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Aliyense wakupikisana ndi inu, osamvera mau anu mulimonse mukamlamulira, aphedwe; komatu khalani wamphamvu, nimulimbike mtima.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Aliyense wotsutsana ndi inu kapena wosamvera zimene mutilamula adzaphedwa. Inu mukhale wamphamvu ndi wolimba mtima!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ali yense wakupikisana ndi inu, osamvera mau anu muli monse mukamlamulira, aphedwe; komatu khalani wamphamvu, nimulimbike mtima.