Joshua 1:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Paliponse pamene muponde phazi lanu, ndakupatsani inu, monga momwe ndidalonjezera Mose.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pali ponse phazi lanu lidzapondapo ndinakupatsani, monga ndinanena ndi Mose.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Paliponse pamene phazi lanu liponde, ndikupatsani monga momwe ndinalonjezera Mose.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pali ponse phazi lanu lidzapondapo ndinakupatsani, monga ndinanena ndi Mose.