Joshua 14:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Potsata zimene Mulungu adalamula Mose, dziko lonse lidagaŵidwa mwamaere kwa mafuko asanu ndi anai ndi theka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kulandira kwao kunachitika ndi kulota maere, monga Yehova adalamulira mwa dzanja la Mose, kunena za mafuko asanu ndi anai ndi fuko logawika pakati.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Madera anagawidwa mwa maere kwa mafuko asanu ndi anayi ndi theka, monga momwe Yehova analamulira kudzera mwa Mose.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kulandira kwao kunacitika ndi kulota maere, monga Yehova adalamulira mwa dzanja la Mose, kunena za mapfuko asanu ndi anai ndi pfuko logawika pakati.