Joshua 14:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Komabe anthu amene anali nane pa ulendowo, adachititsa mantha anthu. Koma ine ndidamvera mokhulupirika Chauta, Mulungu wanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma abale anga amene anakwera nane anasungunutsa mitima ya anthu; koma ine ndinamtsata Yehova Mulungu wanga ndi mtima wanga wonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma abale anga amene ndinapita nawo anachititsa anthu mantha. Komabe ine ndinamvera Yehova Mulungu wanga ndi mtima wonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma abale anga amene anakwera nane anasungunutsa mitima ya anthu; koma ine ndinamtsata Yehova Mulungu wanga ndi mtima wanga wonse.