Joshua 15:18 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsiku lina, Akisayo atafika, Otiniyele adaumiriza mkazi wakeyo kuti apemphe munda kwa Kalebe bambo wake. Tsono Akisa atatsika pa bulu wake, Kalebe adamufunsa kuti, “Kodi ukufuna kanthu?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo kunali, m'mene anamdzera, anamkangamiza mwamuna wake kuti apemphe atate wake ampatse munda; ndipo anatsika pa bulu; pamenepo Kalebe ananena naye, Ufunanji?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsiku lina atafika Akisayo, Otanieli anamuwumiriza mkazi wakeyo kuti apemphe munda kwa Kalebe abambo ake. Pamene Akisa anatsika pa bulu wake, Kalebe anamufunsa kuti, “Kodi ukufuna ndikuchitire chiyani.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo kunali, m'mene anamdzera, anamkangamiza mwamuna wace kuti apemphe atate wace ampatse munda; ndipo anatsika pa buru; pamenepo Kalebe ananena naye, Ufunanji?