Joshua 15:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malire ake akumwera adayambira kumwera kwenikweni kwa Nyanja Yakufa,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi malire ao a kumwera, anayambira ku malekezero a Nyanja ya Mchere, ku nyondo yoloza kumwera;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Malire awo a kummwera anayambira kummwera kwenikweni kwa Nyanja ya Mchere,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi malire ao a kumwera, anayambira ku malekezero a Nyanja ya Mcere, ku nyondo yoloza kumwera;