Joshua 15:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ili ndilo dziko limene mabanja a fuko la Yuda adalandira ngati choloŵa chao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ichi ndi cholowa cha fuko la ana a Yuda monga mwa mabanja ao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Dziko limene mabanja a fuko la Yuda analandira ngati cholowa chawo ndi ili:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ici ndi colowa ca pfuko la ana a Yuda monga mwa mabanja ao.