Joshua 15:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malire akuvuma anali Nyanja Yakufa mpaka kumene Yordani amathira m'Nyanja Yakufa. Tsono malire akumpoto adayambira kunyanjako,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndi malire a kum'mawa ndiwo Nyanja ya Mchere, mpaka mathiriro ake a Yordani. Ndi malire a kumpoto anayambira nyondo ya nyanja ku mathiriro a Yordani;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Malire a kummawa anali Nyanja Yakufa mpaka kumene Yorodani amathira mu Nyanja ya Mchere. Malire a kumpoto anayambira kumene Yorodani amathirira nyanjayo,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndi malire a kum'mawa ndiwo Nyanja ya Mcere, mpaka mathiriro ace a Yordano. Ndi malire a kumpoto anayambira nyondo ya nyanja ku mathiriro a Yordano;