Joshua 17:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zidzukulu za Yosefe zidafunsa Yoswa kuti, “Bwanji ife mwangotigaŵira gawo limodzi lokha la dziko, kuti likhale choloŵa chathu? Ifetu tilipo ambiri chifukwa Chauta adatidalitsa.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo ana a Yosefe ananena ndi Yoswa, ndi kuti, Watipatsiranji cholowa chathu chamaere chimodzi ndi gawo limodzi, popeza ife ndife anthu aunyinji, pakuti Yehova anatidalitsa ndi pano pomwe?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu a fuko la Yosefe anati kwa Yoswa, “Chifukwa chiyani mwatipatsa gawo limodzi lokha la dziko kuti likhale cholowa chathu? Ife tilipo anthu ambiri popeza Yehova watidalitsa kwambiri.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo ana a Yosefe ananena ndi Yoswa, ndi kuti, Watipatsiranji colowa cathu camaere cimodzi ndi gawo limodzi, popeza ife ndife anthu aunyinji, pakuti Yehova anatidalitsa ndi pano pomwe?