Joshua 18:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero Yoswa adafunsa Aisraele kuti, “Kodi mudzadikira mpaka liti kuti muloŵe m'dziko limene Chauta, Mulungu wa makolo anu, adakupatsani?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yoswa anati kwa ana a Israele, Muchedwa mpaka liti kulowa ndi kulandira dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu anakupatsani?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Yoswa anati kwa Aisraeli, “Kodi mudikira mpaka liti kuti mulowe ndi kulanda dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu wakupatsani?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yoswa anati kwa ana a Israyeli, Mucedwa mpaka liti kulowa ndi kulandira dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu anakupatsani?