Joshua 19:10 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mabanja a fuko la Zebuloni adalandira dziko lao, Yoswa atachita maere kachitatu. Dziko limene adalandiralo lidakafika mpaka ku Saridi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo maere achitatu anakwerera ana a Zebuloni monga mwa mabanja ao; ndi malire a cholowa chao anafikira ku Saridi;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maere achitatu anagwera mabanja a fuko la Zebuloni: Malire a dziko lawo anafika mpaka ku Saridi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo maere acitatu anakwecera ana a Zebuloni monga mwa mabanja ao; ndi malire a colowa cao anafikira ku Saridi;