Joshua 19:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mabanja a fuko la Isakara adalandira dziko lao, Yoswa atachita maere kachinai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maere achinai anamtulukira Isakara, kunena za ana a Isakara monga mwa mabanja ao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maere achinayi anagwera mabanja a fuko la Isakara.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maere acinai anamturukira Isakara, kunena za ana a Isakara monga mwa mabanja ao.