Joshua 19:32 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mabanja a fuko la Nafutali adalandira dziko lao, Yoswa atachita maere kachisanu ndi chimodzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maere achisanu ndi chimodzi anatulukira ana a Nafutali, ana a Nafutali monga mwa mabanja ao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera mabanja a fuko la Nafutali.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maere acisanu ndi cimodzi anaturukira ana a Nafitali, ana a Nafitali monga mwa mabanja ao.