Joshua 19:40 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mabanja a fuko la Dani adalandira dziko lao, Yoswa atachita maere kachisanu ndi chiŵiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maere achisanu ndi chiwiri anatulukira fuko la ana a Dani, monga mwa mabanja ao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera mabanja a fuko la Dani.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maere acisanu ndi ciwiri anaturukira pfuko la ana a Dani, monga mwa mabanja ao.