Joshua 20:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu aliyense wopha mnzake mwangozi, osati mwadala, angathe kuthaŵira kumeneko. Motero angathe kupulumuka kwa wofuna kumlipsira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kuti athawireko wakupha munthu osamupha dala, osadziwa; ndipo idzakhalire inu yopulumukirako, kumpulumuka wolipsa mwazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuti aliyense amene wapha munthu mosazindikira osati mwadala azithawirako. Motero adzatetezedwa kwa wolipsira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kuti athawireko wakupha munthu osamupha dala, osadziwa; ndipo idzakhalira inu yopulumukirako, kumpulumuka wolipsa mwazi.