Joshua 21:2 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Aleviwo adafika ku Silo m'dziko la Kanani, nanena kuti, “Chauta adalamula kudzera mwa Mose kuti ife atipatse mizinda yokhalamo, ndiponso atipatse mabusa pozungulira mizindayo, kuti tizidyetsapo zoŵeta zathu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
nanena nao ku Silo m'dziko la Kanani, ndi kuti Yehova analamulira mwa dzanja la Mose kuti atipatse midzi yokhalamo ife, ndi mabusa a zoweta zathu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ku Silo mʼdziko la Kanaani ndipo anati, “Yehova analamula kudzera mwa Mose kuti atipatse mizinda kuti tikhalemo, pamodzi ndi malo odyetseramo ziweto zathu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
nanena nao ku Silo m'dziko la Kanani, ndi kuti Yehova analamulira mwa dzanja la Mose kuti atipatse midzi yokhalamo ife, ndi mabusa a zoweta zathu.